× Home Files Nkhani MisonkhanoZitsanzoToolsAbout
☰ Menu

TIZICHITENGA CHOONADI NGATI NYAMA

Mateyu 28:18, 19

Wanthabwala wina anati: ana akadya chankhuli amasunga kachidutsa kena kuti akawaonetse anzake nkuwagawira aliyese kapisi kakang'ono. Amafuna kuti anzaowo alaweko zabwino zomwe iwo ali nazo. Koma anawa akadya zamasamba samatero ayi.

Mipingo (zipembezo) zonse padzikoli, tingati zikudya zamasamba chifukwa sizimafuna kugawa zomwe zimaphunzitsa, koma ife (Yesaya 43:10) timagawa kwa anthu uthenga wabwino (Mateyo 24:14) omwe uli ngati chidutswa cha nyama. (Mac. 1:8)

Zatsopano

Kodi Mulungu Amaloleza Mitala?

Kodi kutchova juga ndi tchimo?

Zitsanzo

  • Kuchitenga Choonadi ngati nyama

  • online: | hits: x

    Back to top

    “M'patseni Yehova ulemelero
    woyenera dzina lake.”
       - Salimo 96:8.